nya-x-nyanja_rev_text_reg/21/14.txt

1 line
212 B
Plaintext

\v 14 mpanda wa mzinda unali ni maziko 12, pa izo panali maina 12 ya apositoli a mwana wa nkhosa. \v 15 wamene anakamba na ine anali na kopimila kopangiwa na golide kamene anapimila mzinda, makomo na mpanda wake.