Thu Jan 02 2020 18:59:53 GMT+0200 (South Africa Standard Time)
This commit is contained in:
parent
f7f63c508c
commit
ac68d06696
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 5 \v 6 Pambuyo pa izi zinthu ninaona, ndipo tenti ya mboni inaseguliwa ku mwamba. Kuchoka pa malo oyera panachoka angelo 7 onyamula zilango 7. Anavala zobvala zoyera, zonyezimila ndi sashi ya golide yozungulira chifuwa chao.
|
||||
\v 5 Pambuyo pa izi zinthu ninaona, ndipo tenti ya mboni inaseguliwa ku mwamba. \v 6 Kuchoka pa malo oyera panachoka angelo 7 onyamula zilango 7. Anavala zobvala zoyera, zonyezimila ndi sashi ya golide yozungulira chifuwa chao.
|
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 7 \v 8 Imozi mwa zamoyo zinai inapasa angelo 7 mbale za golide 7 za mkwiyo wa Mulungu, zamene zinkhala muyayaya. Tempile inazaziwa na utsi wa ukulu wa Mulungu na mphamvu zake. Palibe amene analobamo mpaka pamene zilango zonse 7 zinatha.
|
||||
\v 7 Imozi mwa zamoyo zinai inapasa angelo 7 mbale za golide 7 za mkwiyo wa Mulungu, zamene zinkhala muyayaya. \v 8 Tempile inazaziwa na utsi wa ukulu wa Mulungu na mphamvu zake. Palibe amene analobamo mpaka pamene zilango zonse 7 zinatha.
|
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 4 \v 5 \v 6 \v 7 Mngelo wa chitatu anathira mbale yake m'misinje na nyenje za manzi ndipo zinasanduka magazi. Ninamvera mgelo wa manzi kukamba ati, "ndinu oyera-amene aliko ndipo analiko, Oyera- chifukwa mwaweruza zinthu izi. Chifukwa anathira magazi ya okhulupilira na aneneri, mwabapasa magazi kuti bamwe; ni zamene bayenera. Ninamvera guwa kukamba ati, "Inde, ambuye Mulungu a mphamvu zonse, chiweruzo chanu ni ca zoona na cholungama."
|
||||
\v 4 Mngelo wa chitatu anathira mbale yake m'misinje na nyenje za manzi ndipo zinasanduka magazi. \v 5 Ninamvera mgelo wa manzi kukamba ati, "ndinu oyera-amene aliko ndipo analiko, Oyera- chifukwa mwaweruza zinthu izi. \v 6 Chifukwa anathira magazi ya okhulupilira na aneneri, mwabapasa magazi kuti bamwe; ni zamene bayenera. \v 7 Ninamvera guwa kukamba ati, "Inde, ambuye Mulungu a mphamvu zonse, chiweruzo chanu ni ca zoona na cholungama."
|
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 8 \v 9 Mngelo wa chinai anathira mbale yake ku zuba, ndipo inapasidwa chilolezo chotentha anthu na muliro. Anatenthedwa na kupya kwakukulu, ndipo ananyoza zina la Mulungu, amene ali na mphamvu pa ziwawa zimenezi. Sibanalape kapena kumupasa ulemelero.
|
||||
\v 8 Mngelo wa chinai anathira mbale yake ku zuba, ndipo inapasidwa chilolezo chotentha anthu na muliro. \v 9 Anatenthedwa na kupya kwakukulu, ndipo ananyoza zina la Mulungu, amene ali na mphamvu pa ziwawa zimenezi. Sibanalape kapena kumupasa ulemelero.
|
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 10 \v 11 Mngelo wa cisanu anathira mbale yake pa mpando wa chilombo, ndipo mdima unaphimba umfumu wake. Anakukuta malilime ao chifukwa cha kuwawa. Ananyoza zina la Mulungu chifukwa cha kuwawa na zilonda, koma anakana kulapa zoipa zomwe anali kuchita.
|
||||
\v 10 Mngelo wa cisanu anathira mbale yake pa mpando wa chilombo, ndipo mdima unaphimba umfumu wake. Anakukuta malilime ao chifukwa cha kuwawa. \v 11 Ananyoza zina la Mulungu chifukwa cha kuwawa na zilonda, koma anakana kulapa zoipa zomwe anali kuchita.
|
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 12 \v 13 \v 14 Mngelo wa nambala 6 anathira mbale yake mu msinje waukulu wa Euphrates. Manzi yake yanauma kupanga njira ya mamfumu yamene yanachokera ku m'mawa. Ninaona mizimu yoipa yomwe yanaoneka monga achule kutuluka mkamwa mwa chinjoka, mwa chilombo na mwa mneneri wa boza. Chifukwa ni mizimu ya ziwanda kuchita milakuli ni zizindikiro. Anali kupita kwa mamfumu a ziko lonse kuwasonkhanisa pamozi kukonzekera nkhondo pa siku lalikulu la ambuye amphamvu zonse.
|
||||
\v 12 Mngelo wa nambala 6 anathira mbale yake mu msinje waukulu wa Euphrates. Manzi yake yanauma kupanga njira ya mamfumu yamene yanachokera ku m'mawa. \v 13 Ninaona mizimu yoipa yomwe yanaoneka monga achule kutuluka mkamwa mwa chinjoka, mwa chilombo na mwa mneneri wa boza. \v 14 Chifukwa ni mizimu ya ziwanda kuchita milakuli ni zizindikiro. Anali kupita kwa mamfumu a ziko lonse kuwasonkhanisa pamozi kukonzekera nkhondo pa siku lalikulu la ambuye amphamvu zonse.
|
|
@ -1 +1 @@
|
|||
\v 9 \v 10 9 ichi chifunika muntu amene ali na nzeru. mitu 7 ni malupili 7 yamene mukazi uyu ankjhalapo. 10 elo ni mamfumu 7. mamfumu yali 5 yanagwa, umozi alipo elo winangu akalibe kubwera, elo pamene azabwera, afunika kunkhalako pang'ono.
|
||||
\v 9 9 ichi chifunika muntu amene ali na nzeru. mitu 7 ni malupili 7 yamene mukazi uyu ankjhalapo. \v 10 Elo ni mamfumu 7. mamfumu yali 5 yanagwa, umozi alipo elo winangu akalibe kubwera, elo pamene azabwera, afunika kunkhalako pang'ono.
|
|
@ -155,6 +155,21 @@
|
|||
"15-01",
|
||||
"15-02",
|
||||
"15-03",
|
||||
"17-title"
|
||||
"15-05",
|
||||
"15-07",
|
||||
"16-title",
|
||||
"16-01",
|
||||
"16-02",
|
||||
"16-03",
|
||||
"16-04",
|
||||
"16-08",
|
||||
"16-10",
|
||||
"16-12",
|
||||
"17-title",
|
||||
"17-01",
|
||||
"17-03",
|
||||
"17-06",
|
||||
"17-08",
|
||||
"17-09"
|
||||
]
|
||||
}
|
Loading…
Reference in New Issue