\c 14 \v 1 Tambilani umweyo ana utofu pachikhulupililo, koma muchachitisane naye makani pabzvinthu bzvaaninga achikumbuka. \v 2 Munngo munthu anachikhulupililo chakudya bzventse, koma munango analibe kulimba andodya muliwa wamasamba basi.