\v 26 Adaimba nyimbo, adabuda adaenda kupili la Olive. \v 27 Yesu adti kwaiwo, ''Imwe mwense muzanditawa nakufuna kwakuti kunanembewa; ndichamenya kabusa wa mbelele apo dzizamwazika. Apo mumambuyo mwakulamuka kwangu. ndichatsogolalela Galillea.