nya-x-nyanja_1pe_text_reg/04/17.txt

1 line
317 B
Plaintext

\v 17 \v 18 \v 19 koma chiweluzo chiyamba na nyumba yamulungu.ikayamba na ise .nanga imwe,amene sinmumavelela mau yamulungu.kapena muntu oyela azavutikila kungena kumwamba nanga chizankala bwanji kuli muntu amene saziba mulungu?lekani amene bavutika kamba kamulungu baike moyo wao kuokulupilika anapanga vonse bwino.