nya-x-nyanja_1pe_text_reg/03/01.txt

1 line
215 B
Plaintext

\c 3 \v 1 Mwaichi' imwa okwatiwa nvelelani amuna anu. Chitani ichi nangukuti amuna anu samvelela mau, an'nga tembenuke nangukulibe mau, mukupitila muzochita za bakazi bao. \v 2 Bazaona zochita zao zabwino za ulemu.