nya-x-nyanja_1pe_text_reg/03/18.txt

1 line
379 B
Plaintext

\v 18 Klistu naye anavutika chifukwa chamachimo yatu. Eve oyela anatifela, enze oyela, kuti atibwelese kwa Mulungu. Anapaiwa kumubili koma anauka kumuzimu. \v 19 Mwa muzimu, anapita kulalikila kuba mundende. \v 20 Sibana nvelele pamene Mulungu anaba yembekezela mumasiku yanowa. Mumasiku yopanga chi boti na Mulungu ana pulumusa bantu ban'gono-moyo zili chabe 8. kupita mumanzi.