nya-x-nyanja_1pe_text_reg/03/10.txt

1 line
271 B
Plaintext

\v 10 Amene akonda umoyo wabwino nakufuna kuona zabwino asiye kunena nalilime zoipa zamaboza. \v 11 Achoke ku choipa achite chabwino, afunne mtendele aupilikise. \v 12 Menso yamulungu yaona oyela namatu yake yamaba nvela. Koma chinso cha Mulungu chimaukila ochita zoipa.