nya-x-nyanja_1pe_text_reg/04/03.txt

1 line
484 B
Plaintext

\v 3 \v 4 \v 5 \v 6 pakuti ntawi yabwino inapita yamene mulungu anapasa osamuziba achiti zamene banalikufuna kutibachite-,kukumbwa,kukonda,kukolewa,kukumbwa kumbwa,nakudyela muziko,nakupennpela toumba banayamba tosayenela.aba bantu nibodabwa pamene baona imwe simukanbako voipa vamene bakamba,bama yambakukamba voipa pali imwe.bayembekeze wamene aza weluza bamoyo naba kufa.ndiye chifukwa mau yana lalikiwa kuli bakufa.nangukuti bannaba weluza kumubili,koma bazankala namoyo kumuzimu.