nya-x-nyanja_1pe_text_reg/03/01.txt

1 line
224 B
Plaintext

\c 3 \v 1 Mwaichi' imwe okwatiwa nvelelani ba muna banu. Chitani ichi nangukuti amuna banu samvelela mau, an'nga tembenuke nangu kulibe mau, mukupitila muzochita za bakazi bao. \v 2 Baza ona zochita zao zabwino za ulemu.