nya-x-nyanja_rev_text_reg/01/01.txt

1 line
421 B
Plaintext

\c 1 \v 1 \v 2 \v 3 Ili ni vumbuluso la Yesu Kristu lamene Mulungu anamupasa kuti aonese akapolo ake zamene zizacitika manje-manje. Anazionesa kupitira mwa mngelo wake kwa Yohane. Yohane anacitira umboni mau a Mulungu na pa umboni operekedwa wa Yesu Khristu, zinthu zonse zamene anaona. Ni odala amene abelenga mokweza, na amene amvera mau ya uneneri, na bamene bagonjera zamene zinalembedwamo, cifukwa nthawi ili pafupi.