nya-x-nyanja_rev_text_reg/20/04.txt

1 line
342 B
Plaintext

\v 4 ninaona mipando. wamene anankhalapo ni baja bamene banapasiwa mphamvu zoweruza. ninaonaso mizimu ya baja bamene banajubiwa mitu kamba ka umboni wa yesu na mau ya mulungu. sibanapembeze chilombo na chifano chake, elo banakana kulandira chizindikiro pa mpumi kapena pa manja yawo. banauka, ndipo banalamulira na yesu khristu kwa zaka 1000.