nya-x-nyanja_rev_text_reg/17/09.txt

1 line
189 B
Plaintext

\v 9 Ici cifuna maganizo anzelu. Mitu 7 ni malupili 7 pamene mkazi ali nkhezi. \v 10 Pali na mafumu 7. mafumu 5 bagwa, m'mozi wasala, na wina akalibe kubwela; akabwela azankhalako pang'ono.