nya-x-nyanja_rev_text_reg/08/08.txt

1 line
221 B
Plaintext

\v 8 \v 9 Mngelo wa chiwiri analiza lipenga lake, ndipo chinthu china chachikulu monga phiri chinaponyedwa mnyanja. Gawo lina la manzi inankhala magazi, zina mwa nyama za m'manzi zinafa, ndipo ma bwato ambiri anaonongeka.