nya-x-nyanja_rev_text_reg/03/14.txt

1 line
210 B
Plaintext

\v 14 \v 15 \v 16 Kwa mngelo wa mpingo wa ku Laodicea lemba: Aya ni mau ya ma Amen, mboni ya zoona na yodalilika, olamulira chilengedwe cha Mulung u. Niziba zamene mwachita, kuti sindinu otentha kapena ozizira.