nya-x-nyanja_rev_text_reg/22/08.txt

1 line
347 B
Plaintext

\v 8 \v 9 ine, yohane, ndine wamene ninamvera na kuona zinthu izi. pamene ninamvera na kuona, ninagwa pansi ku mapazi ya mungelo kuti nimupembeze, na mungelo wamene ananilangiza izi zinthu. anakamba kwa ine, "usacite tero! naine ndine kapolo kwati iwe, na abale bako baneneri. na bonse bamene bamvera mau yamene yali mu buku iyi, pembeza mulungu!"