nya-x-nyanja_rev_text_reg/20/01.txt

6 lines
904 B
Plaintext

<<<<<<< HEAD
\c 20 \v 1 Ndiponso ni naona mungeli aseluka ku mwamba. Enze na fungulo ya ku chimugodi chosasila, ndipo enze na chi unyolo chikulu mu kwanja yake. \v 2 Ana gwila chilombo, njoka yakudala, ali mujelekezi, olo satana, naku mumanga zaka 1000. \v 3 Ana chiponya mu chimogodi chosasila, ana komako naku valikiza. Uku kwenze kuti asa pitilize kunama ma ziko mpaka pamene zina sila zaka 1000. Kuchoka apo, afunika amangusuliwe paka ntawi kang'ono.
=======
\c 20 \v 1 \v 2 \v 3 ninaona mungelo wamene anachoka ku mwamba. anali na makiyi ya kumugodi opanda kolekezera, elo anali na tcheni ikulu maningi mumanja mwake. anagwira chinjoka, chamene ni mudyerekezi, kapena satana, na kumumanga kwa zaka 1000. anamuponya mu chimugodi, elo anavalapo. banachita izi kuti asanamize futi maiko mpaka zaka 1000 zisile. pambuyo pake bazamumasula pangóno chabe.
>>>>>>> 1dadec7d9b0a000d2dba1dd240dc74f95bb143b5