nya-x-nyanja_rev_text_reg/19/01.txt

1 line
390 B
Plaintext

\c 19 \v 1 \v 2 zitapita izi zinthu ninamvera chamene chinamveka kwati ni mau yampamvu ya banthu bambiri kumwamba kukamba ati, "hallelujah. chipulumuso, ulemelero na mpamvu zikhale kwa mulungu wathu. chiweluzo chake ni chachilungamo na choona, cifukwa aweluza hule ya mpamvu yamene inasokoneza ziko la pansi na nkhalidwe yake ya uhule. wabwezera magazi ya akapolo ake, yamene iye anakhesa."