nya-x-nyanja_rev_text_reg/14/13.txt

1 line
190 B
Plaintext

\v 13 Ninamva mau kuchoka ku mwamba kukamba ati, "Lemba izi: Odala ni anthu amene anafa mwa ambuye." "Inde," ukamba mzimu,"kuti akapumule ku zolemesa zao, chifukwa nchito zao zizabalondola."