nya-x-nyanja_rev_text_reg/03/05.txt

1 line
214 B
Plaintext

\v 5 \v 6 Wamene apambana azapasiwa zobvala zoyera, elo sinizachosa dzina lake mu buku la moyo, ndipo nizakamba za dzina lake kwa atate, na angelo ao. Lekani amene ali na matu amvere zamene mzimu akamba ku mipingo.