nya-x-nyanja_rev_text_reg/01/07.txt

1 line
261 B
Plaintext

\v 7 \v 8 Onani, azabwera mu makumbi; ndipo diso lililose lizamuona, kuikapo naonse bamene banamulasa. Ziko lonse lizalira chifukwa cha yeve. Inde, Amen. "Ndine oyamba na osiliza," akamba ambuye Mulungu, "amene analiko, aliko, elo azankhalako, wa mpamvu zonse."