nya-x-nyanja_rev_text_reg/12/03.txt

1 line
417 B
Plaintext

\v 3 Kunkopa kunali cholangiza chinangu chamene china onekela kumwamba: Onani! Kunali chilombo chikulu cha red chamene chinali na mitu seven na nsengo zili kumi, komanso kunali visoti va ufumu vinali seven pa mitu pake. \v 4 Muchila wake una pyanga nyenyezi mumwamba naku yaponya pansi pa ziko. Chilombo ichi chinaimilila pamene panali muzimai wamene anali kuyembekezela kubeleka, mwakuti akabeleka, chidye mwana uja.