nya-x-nyanja_rev_text_reg/09/13.txt

1 line
410 B
Plaintext

\v 13 Mngelo wa namba 6 analiza lipenga lake, ndipo ninamva mau ochokera mu nyanga ya pa guwa la golide yomwe ipezeka kwa Mulungu. \v 14 Liu linanena na mngelo wa nambala 6 yemwe anali na lipenga, "masula angelo anai omwe niomangiwa pa msinje waukulu wa Euphrates." \v 15 Angelo anai omwe anakonzedwera nthawi imenei, siku limeneli, mwezi umeneo na chaka chimenechi, anamasulidwa kuti aphe gawo lina la anthu.