nya-x-nyanja_rev_text_reg/07/15.txt

1 line
418 B
Plaintext

\v 15 Pa chifukwa ichi, ali pa maso pa mpando wa Mulungu, ndipo amiupembeza usana na usiku mu nyumba yake. Iye wamene ankhalaa pa mpando wa chimfumu azaika tenti yake pa iwo. \v 16 Sazamveranso njala, kapena kumvera ludzu. Dzuwa sizawagwesa, kapena kutenthewa. \v 17 Chifukwa mwana wa nkhosa pakati pa mpando azankhala mbusa wao, ndipo azawapereka ku malo a manzi ya moyo, ndipo Mulungu azapukuta misozi mu menso yao."