nya-x-nyanja_rev_text_reg/15/02.txt

1 line
245 B
Plaintext

\v 2 Ninaona chamene chinaoneka monga nyanja ya galasi yosakaniza na muliro. Amene anaimilira pa mbali ya nyanja ni aja amene anapambana chilombo na fano lake, na nambala yamene iimilira zina lake. Anali na mitoliro yamene anapasidwa na Mulungu.