nya-x-nyanja_rev_text_reg/19/09.txt

1 line
396 B
Plaintext

\v 9 mungelo anakamba kwa ine, "lemba izi: ni odala amene aitaniwa ku pwando la ukwati wa mwana wa nkhosa." anakamba futi kwa ine ati, "aya ni mau ya zoona ya mulungu." \v 10 ninagwa pansi pa mapazi ake kuti nimupembeze, koma anakamba kwa ine ati, "osachita tero! naine ndine kapolo kwati iwe na abale ako amene ali na umboni wa yesu. pembeza mulungu, pakuti umboni wa yesu ni muzimu wa uneneri."