nya-x-nyanja_rev_text_reg/11/13.txt

1 line
274 B
Plaintext

\v 13 Pa ntawi ija kunzankala chivomezi, ndipo imozi ya magawo kumi ya muzinda izagwa. Bantu bali 7, 000 baza paiwa mu chivomezi, ndipo bopulumuka baza yopa naku pasa ulemelero kuli Mulungu waku mwamba. \v 14 Soka ya chibili yachoka. Ona! soka ya chitatu ibwela mwamu sanga.