nya-x-nyanja_rev_text_reg/08/06.txt

1 line
277 B
Plaintext

\v 6 Angelo 7 omwe anali na malipenga anakonzeka kuti alize. \v 7 Mngelo oyamba analiza lipenga lake, ndipo panali mvula ya mphepo, moto yosakaniza na magazi. Inaponyedwa pa dziko la pansi kwakuti gawo lina linatenthedwa, gawo la mitengo inapya, ndi udzu onse obiliwira unapya.