nya-x-nyanja_rev_text_reg/11/13.txt

1 line
272 B
Plaintext
Raw Normal View History

\v 13 Pa ntawi ija kunzankala civomezi, ndipo imozi ya magawo kumi ya mzinda izagwa. Bantu bali 7, 000 baza paiwa muchi vomezi, ndipo bopulumuka baza yopa naku psa ulemelero kuli Mulungu waku mwamba. \v 14 Soka ya chibili yachoka. Ona! soka ya chitatu ibwela mwamu sanga.