\v 10 \v 11 \v 12 Bamene bankala pa ziko ya pansi baza kondwela pali yeve naku sangalala. Baza pasana na mpaso chifukwa aba baneneli babili bana vutisa bantu benzo nkala pa chalo. Koma pakapita ma siku yatatu na imozi yo juba pakati mpepo yochoka kuli Mulunguiza ba ngena, ndipo baza imilala pa ma pazi yao. Kuyopa kukulu kuzagwera bonse bazaba ona. Ndipo bazamvela liu ikulu kuchoka ku mwamba kuba uza, "Bwera pamwamba pano!" Ndipo baza yenda kumwamba mu kumbi, pamene badani babo bayanganila.