\v 10 nikufunsani za mwana wanga onesimus, wamene ninabala mu zingwe. \v 11 chifukwa poyamba anali opanda nchito kwa inu, koma sopano ali na nchito kwa inu na ine. \v 12 namutuma kwa inu, wamene ni mutima wanga. \v 13 ninakakonda kumusunga pamozi na ine kuti anigwirire nchito m'malo mwa inu, pamene nili mu zingwe kamba ka uthenga wabwino.