\v 7 Yosefe anaona babele bake nakubaziba ana zibisi kuli beve naku kamba nabo mo limba anakamba nao, mwacokela kuti? Banakamba kuli tacokela ku Kanani kubwela kugula vo kudya. \v 8 Yosefe anabaziba ba bale bake, koma beve sibana muzibe.