nya-x-nyanja_gen_text_reg/20/04.txt

1 line
225 B
Plaintext

\v 4 Manje Abimeleki sanabwele pafupi na eve ndipo anakamba kuti, "Ambuye, munga paye ziko yalungama? \v 5 Sanakambe eve eka kwa ine, ' ninabadwa naye, 'Nacita ici mwa ulemu wa mtima wangu na kupanda cifukwa kwa manja banga."