nya-x-nyanja_gen_text_reg/06/05.txt

1 line
221 B
Plaintext

\v 5 Yawe anaona kuti kuyipa mtima kwa munthhu kuli kukula pa ziko, ndipo maganizo yao ya mitima yao yanali yoipilathu nthawi zonse. \v 6 Yahova cinamubaba kuti anapanga munthu pa ziko, ndipo anamvela kuipa mumutima wake.