nya-x-nyanja_gen_text_reg/25/21.txt

1 line
290 B
Plaintext

\v 21 Isaki anapemphelera mkazi wake kwa Tehova cifukwa senze kubala, ndipo Yehova anayankha pemphero yake,ndipo mkazi wake Rabekah anakhala navumo. \v 22 Bana banavutana muvumo mwake , ndipo anakamba kuti, " Cifukwa ni chani ivi vicitika kuli ine?" Ndipo anayenda kufusa Yehova pali ivi.