nya-x-nyanja_gen_text_reg/25/17.txt

1 line
261 B
Plaintext

\v 17 Izi ndiye zaka zamoyo wa Ishumaele, zaka 137, ndipo iye anamwalira, ndipo anatengawa kuli bathu bake. \v 18 Ndipo banakhala, kuyambira ku Havilah na kufika ku Ashhuri, yamene ili pafupi na Egipito, monga iyenda ku Assirila. bankhala boyambana bekha bekha.