nya-x-nyanja_gen_text_reg/42/14.txt

1 line
403 B
Plaintext

\v 14 Yosefe anababuza kuti, "Ndiye vamene naku uzani. ndimwe oipa. \v 15 Pali ici muza yesewa na moyo wa falabo, simuzacoka pario, koma cabe ngati mubale wanu mung'onu abwere kuno. \v 16 Tmani umozi mumusiye akatenge mubale wanu. Muzasala mundende, kuti mau yanu yayesewe. Kuona ngati muli cazo ona muli imwe. Ngati siivo, pa moyo wa Falao ndimwe oipa zo ona. \v 17 Anaika bonse mundende musiku yatatu.