nya-x-nyanja_gen_text_reg/42/01.txt

1 line
471 B
Plaintext

\c 42 \v 1 Ndipo Yakobo anaona kuti munali vakudya mu Egipito. Anakamba kuli bana bake bamuna. Cifukwa nichani muyang'ana yang'ana? \v 2 Anakamba, onani apa, namvera kuti kuli vakudya mu Egipito, Yendakoni kuti mukati gulile kuti tinkhale namoyo tisamwalile. \v 3 Abale bake ba Yosefe bali banayenda kugula vakudya ku Egipito. \v 4 Koma Yakobo sana tume benjamini, mubale wake wa yosefe, pamozi na bale bale popeza anakamba kuti, "Niyopa kuti voipa vingacitike pali yeve.