nya-x-nyanja_gen_text_reg/03/09.txt

1 line
288 B
Plaintext

\v 9 Yahova Mulungu anaitana mwamuna nakumufunsa kuti, " Uli kuti?" \v 10 Mwamuna anayankha kuti, " Nakumverari mu munda, nenze na mantha, ndaba nenze cinthako. Nenze nabisama." \v 11 Mulungu anakamba, " Nindani akuuza kuti wenze cinthako? Kodi wadya mumtengo nina kulesa kuti osadyamo?"