nya-x-nyanja_gen_text_reg/42/29.txt

1 line
376 B
Plaintext

\v 29 Anayenda kwa Yakobo, tate wo muziko ya Kanani ndi kumu uza vonse vinaba citikila. Banakamba kuti. \v 30 Munthu, mbuye waziko, an anakamba, naise moka lipo nakuti ona monga ndise oipa muziko. \v 31 Takamba kuli yeve, ndife bamuna bazona, sindife boipa. \v 32 Tili abale tyovu, bana ba atate bathu, umozi salimoyo, ndipo ndipo mung'ona lelo ati na batate muziko ya Kenani.