nya-x-nyanja_gen_text_reg/35/06.txt

1 line
377 B
Plaintext

\v 6 Mwaicho Yakobo anafaka ku Luz (amene inali Bethel), yamene inali kumalo yaku Kanaani, eye na bonse bantu bamene banali naye. \v 7 Anamanga guwa kuja na kupasa Mulungu anazi onesa kuli eve pamene anali kutaba ku chokela kuli mu bale wake. \v 8 Deborah, wachinto wa Rabekal, anafa. Anashikiiwa ku Bethel pansi pa mutengo wathundu, mwaicho bana itana malo yaja Allon Bakuthi.