nya-x-nyanja_gen_text_reg/29/01.txt

1 line
502 B
Plaintext

\c 29 \v 1 Pamene apo Yakobo anayenda paulendo wake na kufika ku malo ya bantu ba ku maba. \v 2 Pamene anayangana, anaona chisime mumunda, na, onani, magulu yatatu ya mbelele yanali gone mumbali. chifukwa cikuchoka mu chicime ichi banali kumwesalamo mbelele, na mwala unali pakamwa pachisime unali ukulu. \v 3 Pamene yonse magulu mbelele yanakumana paja, na bachibeta banali kuchosa mwala pakamwa pachisime na kupasa mbelele manzi, naku bwezapo chimwala futi pakamw pachisime, nakuchibweza mumalo yake.