nya-x-nyanja_gen_text_reg/24/26.txt

1 line
269 B
Plaintext

\v 26 Mwamuna anagwada na kuyamika Yehova. \v 27 Anati, adalisike Yehova Mulungu wa bwana wanga Abrahamu, wamene sanakane ku kulupilika kwa chipangano ndi chifundo chake mwa bwana wanga. Koma monga ine , Yehova anisogolela munjila ya kunyumba ya ba bale ba bwana wanga.