nya-x-nyanja_gen_text_reg/23/12.txt

1 line
256 B
Plaintext

\v 12 Pamene apo Abrahamu anagwanda pa manso pa bantu a mudziko. \v 13 Anakamba na Efron mukuvelela kwa bantu bamu dziko, kuti, koma ngati mufuna, napapata niveleni. Nizalipila zamunda. Tengani ndalama kuchokela kuli ine, ndipo niza ika wokufa wanga kuja."