nya-x-nyanja_gen_text_reg/23/14.txt

1 line
441 B
Plaintext

\v 14 Efron anayankha Abrahamu, kuti \v 15 " Chonde, bwana wanga, niveleni ine. Ka malo ka nthaka ko kwanila muyeso wafolo handredi ma shekeli ya siliva, ni cani ici camene cili pakati pali ine na iwe? Ika wakufa wako." \v 16 Abrahamu anavelela kuli Efulon ndipo Abrahamu ana pimila Efulo muyeso wa siliva wamene ana tomola pokamba milandu nabana bamuna ba Heti, Folo handiledi ma shekelo ya siliva, kulinga na kapimidwe ka bwino kama londa.