|
\v 12 Pamene apo Abrahamu anagwanda pa manso pa bantu a mudziko. \v 13 Anakamba na Efron mukuvelela kwa bantu bamu dziko, kuti, koma ngati mufuna, napapata niveleni. Nizalipila zamunda. Tengani ndalama kuchokela kuli ine, ndipo niza ika wokufa wanga kuja." |