nya-x-nyanja_gen_text_reg/42/23.txt

1 line
368 B
Plaintext

\v 23 Sabanazibe kuti Yosefe anabamwesesa, cifukwa panali omasulila pakati kao. \v 24 Anacoka pali beve ndipo analila. Ana bwelela kuli beve nokamba nao. Anatenga simiyoni nakumu manga menso yao. \v 25 Yosefe ana lamulila ba nchito bake kuti ba zuze machola na vakudya, ndikuika ndalama za munthu alibonse mucola cake, ndi ku bapasa vose vofunika paulendo. zinacitika.