nya-x-nyanja_gen_text_reg/44/20.txt

1 line
387 B
Plaintext

\v 20 Tinakamba kwa mfumu, "Tilinayo atate, ba chikulile na mwana wamu ukote wayo muny'ono. Koma mbale wake anafa, ndipo eve aka ndiye anasalapo ya ba mayi bake, na batate bake bomukonda. \v 21 Ndipo munakamba kuli ba chinto banu,, mu bweleseni kiuli ine ni muone! \v 22 Kuchoka apo tinakamba kuli ba bwana banga, 'Munyamata sangasiye ba tate bake. Ngati abasiya batate bake bazamwalila.