nya-x-nyanja_gen_text_reg/50/04.txt

1 line
463 B
Plaintext

\v 4 Pamene masiku olila ana sile, Yosefe anakamba ku nyumba ya Falao, anakamba, "ngati manje napeza mwai mu meso yako, napapata nikambileni kuli Falao kukamba kuti. \v 5 Ba tate banani Lepisa kukamba, "Ona nili pa fupi kufa. Ne shikeni mu manda mwamene niza zikumbila ine neka muziko ya Kenaani. Ukudiye muzanishika ine." Manje lekani ine niyende nika shike ba tate banga. Ndiponso nizabwelela. \v 6 Falao anayanka, "Enda ka shike ba tate bako ba, banani lapisa.