nya-x-nyanja_gen_text_reg/47/25.txt

1 line
279 B
Plaintext

\v 25 Bana kamba kuti, " Wapulumusa umoyo wantu. Tipeze chisomo mumenso yanu. Tizakhala ba chito ba Farao." \v 26 Ndipo Yosefe ana iyika lamulo yokokhewa mudziko la igipito kufikila lelo, kuti chachisanu chimozi ndi cha Farao. Malo chabe yabasembe niyamene Siyanakhale ya Farao.